Article
Kodi mwaimva iyi? Ngati Zili zoona anthu ambiri Mumangidwa

Kodi mwaimva iyi? Ngati Zili zoona anthu ambiri Mumangidwa

Phokoso pa Kugonana ndi Mlandu Waukulu – A Lawyer Maurice wafotokoza motere

Maurice wapereka chenjezo lamphamvu kwa ma banja omwe amachita phokoso lalikulu akamachita chikondi (kugonana), ponena kuti khalidwe limenelo ndi mlandu ndipo lingawachititse kuti akumane ndi mavuto a malamulo.

Polankhula pa Podcast ya United Showbiz Maurice anafotokoza kuti ngakhale kuli kusonyeza kumva kukoma kapena kukondwa pa nthawi ya kugonana kwachilengedwe, phokoso lopitilira Myezo monga kufuwula mokweza ndi chinthu chokwiitsa anthu ena komanso kusokoneza mtendere wawo.

Iye anatsimikizira kuti ndizololedwa kuti ma banja azisonyeza kumva kukoma kapena kukondwa pomafuula mofatsa pa nthawi ya chikondi, koma adzipewa phokoso lochulukira ndipo azichita izi mwaulemu kwa anzawo apafupi monga oyandikana nawo.

“Simuyenera kufuwula. Kusokoneza mtendere Komanso kumaphatikizapo kupanga phokoso, ndipo aliyense ali ndi ufulu wokhala mwamtendere m’madera awo.”

Lawyer yu anapitiliza kufotokoza kuti kupanga phokoso lalikulu pa kugonana kungaganizidwe ngati kuswa ufulu wa anthu ena amene akumangozimvetsa popanda chilolezo chawo, makamaka m’madera omwe anthu amakhala pafupi kwambiri.

Kuonjezera apo , iye anakumbutsaso makolo ena omwe ali ndi khalidwe losamba limodzi ndi ana achichepere kuti asiye kusamba kapena kuvala m’maso mwa ana awo pakuti ndizolakwika Ndipo ponena za chitsanzo cha milandu ina yomwe inachitikapo ngati yomweyi iye anafotokoza kuti

Mlandu ngati omwewu umu ndim’mene zinakhalira kuti Bambo wina agwidwe ndi kutsekeledwa m’ndende chifukwa chosamba limodzi ndi mwana wake wa Mkazi ndipo mwana wa mkaziyo zinamuopsya zomwe anaonazo mpaka anayamba kuuza anzake kenako nkhani ija inatchuka mpaka ku court Bambo yo ndikutsekeledwa

Admin Jeffrey

Comment Below

19 Comments

Bless

Izi ndye chaaaaa 😂😂😂😂😂😂

Chikubusy mussah

😆😆😆nice song

MALIUCE

Aaaaaaa 😅😅

Mm

🥱

Mozy frack

Eshiiii 😂

Kumitawa Seba

Mmmmmm iyiso nde iti sound ija ipeleka chilimbikiso chokwanila kwamamuna

Immaculate Mbera

Zuoneka ngat zopanda pake kwa anthu omwe simunakumane nazo mukadzakumana nazo mudzanena😂ndipo or tulo timatheratu ohoo

Jimmy songeya

Ndizoona zimasokoneza ena mukaganizidwe nthawi yomwe akupumulira kuntchito zina

Mussa keys

Zokoma

Paul

Ok

Symon

Awa ndi malamulo aku malawi ubwino wake tonse tikapuma kumwamba basi

MIKE KANDODO

Kupanga phokoso kutha kukupangitsa kut ugwidwe ngt ukupanga zimenezo ndi mkazi wamwini

Yekhaya

Angogula ma head sets kuti asamave kukuwa.... CHOTI adziwe kukuwa ndi feeling..........chimakhala chimidzi chani enadi anaphudzila koma adakali ndi life yachimidzi 😃😃😃

Uzzy

Km kujoweni kuno nde mungatenge dziko losetu😂🤣

Memori fostino

Km ngt Kuli kuphwanya ufulu wa A2 ena ndy lamulo limenero libwere lizagwile ntchito kwambr kuno Ku SA 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣 Kuli ntchito kuno osat masewera

Itz Hasco

Aaah nde ikoma bwanj popanda phokoso🤣

Kuwani KINGCRAB

🤣🤣🤣makosana ndima lawyer awo tsopano

Gonzalo Nunez

Anthu a malamulo kuchulusa zochita 😂😂 amzao tisasangalale shuputi

upload your music with us to get maximum reach out!